Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

 

YEHOVA Mlungu wathu,
Amene mumapatsa
Zipatso za chikondi
Polenga anthu anu,
Mupatse awa ‘ŵiri
Mitima yokondwetsa,
Yofana m’munda muja
Munayendamo kale.

Mbuyathu wokondedwa,
Pokhala m’dziko muno
Munadza ku ukwati,
Naŵadalitsa onse;
Ukwatiwu mukonze,
Mukhale nafe pano;
Iwowa m’ŵadalitse
M’chifundo chanu chonse.

Ndi Mzimutu Woyera
Mufike nayo mphamvu,
Mukatsangane nawo
Akupangana omwe;
Mupatse ’wo chisomo
Chokometsetsa mtima;
Chikuletu chikondi
Chitsazo nchanu chomwe.

Mulungu mwa Atatu,
Atate, Mwana, Mzimu,
Tikhaletu wokondwa
Ndi Inu m’chiyanjano;
Titama Inu Mlungu,
Wokonda ife ndinu;
M’ulendo wathu wonse
Tiyende m’chikondano.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 563 Ndipo Mwana uyu Yesu
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version