Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

  1. Home   »  
  2. Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

 

MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
Ndi mtima wokondwera kuloŵa m’nyumbayi;
Chifukwa cha zabwino mwatichitirazi
Tikukuyamikirani leroli.

Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
Mwatimangira ’fe kuno kachisi wanuyu!
Ndi ulemerero wanu mudzaze m’nyumbayi;
Muyeretse, mudalitse munomu.

Tikondwa tonse ndikukuthokozani ’Nu
Poyamba kupemphera ndikuimbira ’mu;
Mommuno nsiku zonse mukhale nafetu,
Monga ndi angelo anu m’Mwambamo.

Ikhale ngati nyali yoŵala nyumbayi,
Yakutsogoza onse ophunthwa m’mdima bii;
Akunja ndi Akristu m’ŵapulumutse ndi
Kuunika kotuluka munomu.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version