Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

  1. Home   »  
  2. Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

 

MBUYE mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Utsani anthu akufa
Ndi mawu a mphamvu.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito zonse zanu!
Tauzirani pa ife
Ndi mweya wa Mzimu

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’mitimamo!
Mumvetse njala kwa Inu—
Mutikhutitsenso.

Mbuye mtsitsimutse
Ntchito m’kati mwa anthu!
Chikondi chawo chikule
Muchikolezetu.

Mbuye mtsitsimutse!
Mawu alimbike,
Pamene aphunzitsidwa
Onsewa amvere!

Mbuye mtsitsimutse!
Mzimu adzazetu!
Kwa ife kudzakhala mwayi,
Kwa Inu ulemu.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 1470 Chikondi cha Mbuyathu
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version