Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

  1. Home   »  
  2. Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

 

MKATI mwa zovuta zathu
Yesu aitana ife,
Tsiku lonse amanena:
“Tsata Ine mkristu iwe.”

Kale ophunzira ake
Namvanso kunyanja kwawo,
Zinthu zonse anasiya
Kukatsata Mbuye wawo.

Yesu atiuze ife;
Tikakonda chuma chokha,
Ati Yesu; “Mwana wanga,
Undikondetu koposa.”

Mwachimwemwe, mwachisoni,
Pogwiritsa ntchito zonse,
Aitana Mpulumutsi
Kuti tizimkonda tonse.

Yesu ayitana ife;
Mbuye, mutimvetse ndithu,
Tipereke mtima wathu,
Tikondane lero ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 424 Yesu, mndiyeretse,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 380 Ndipyola kodi chikhwawa
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version