Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

  1. Home   »  
  2. Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

 

MKATI mwa zovuta zathu
Yesu aitana ife,
Tsiku lonse amanena:
“Tsata Ine mkristu iwe.”

Kale ophunzira ake
Namvanso kunyanja kwawo,
Zinthu zonse anasiya
Kukatsata Mbuye wawo.

Yesu atiuze ife;
Tikakonda chuma chokha,
Ati Yesu; “Mwana wanga,
Undikondetu koposa.”

Mwachimwemwe, mwachisoni,
Pogwiritsa ntchito zonse,
Aitana Mpulumutsi
Kuti tizimkonda tonse.

Yesu ayitana ife;
Mbuye, mutimvetse ndithu,
Tipereke mtima wathu,
Tikondane lero ndithu.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 367 Nonse okhala pansipa,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 309 Mwa Mzimu mulowe mumitima yathu,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version