Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 401 A MULUNGU,

  1. Home   »  
  2. Hymn 401 A MULUNGU,

Hymn 401 A MULUNGU,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 401 A MULUNGU,

 

A MULUNGU,
Munatuma Yesuyo,
Mwana wanu Yekhayo.

Anabadwa,
Anabadwa motere,
Monga mmphaŵi m’kholamo.

Anakonda
Anakonda anthuwo,
Naŵapulumutsanso.

Anafera,
Anafera m’mtandamo,
Anafera ifenso.

Anadzuka
Anadzuka m’mandamo,
Anatenga moyowo.

Anakwera,
Anakwera m’Mwambamo
Kwa Mulungu ’Tatewo.

Adzabwera,
Adzabwera Iyeyo
Tsiku lomalizalo.

Aleluya,
Aleluya Yesuyo,
Tizitama dzinalo.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version