Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

  1. Home   »  
  2. Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

 

INU Mulungu, tikuyamikani;
Tivomereza ndinu Ambuyathu;
Ponse, atate, akugwadirani,

Nanu akukuzani amithenga,
Nanu zam’mwamba ndi zamphamvu zake,
Nanu angelo a mitundu yonse
Akuimbirani:

“Mbuye Woyera! E, Woyera nokha!
Mbuye Woyera! Mbuye wa makamu!
Ponse ulemu wanu ndi wodzaza;
Pansi ndi Kumwamba.”

Inu atumwi akumweka aja,
Ndi aneneri oyanjana omwe;
Ndi aunyinji anakuferani;
Akuyamikani.

Mpingo Woyera! wa kwa anthu onse;
Ukumverani, Mfumu ndi Atate,
Mwana woona wa ulemu wonse,
Mzimu, Nkhoswe yemwe.

Khristu Mfumuyo yaulemerero!
Mwana wosatha wa Atate ndinu!
Simunanyoza mimba ya Namwali;
Potipulumutsa.

Imfa mutagonjetsa ndi zoŵaŵa.
Njira munatsegula tikaloŵe;
Momwe mukhala Inu ndi Atate;
Mu ulemerero

Kumva milandu yathu mudzabwera;
Mutithandize, atumiki anu;
Mwatiwombola nawo mwazi wanu;
Mutipulumutse.

M’tiŵerengere
M’Mwamba ndi oyera;
Mutidalitse, ndi’fe anthu anu;
Moyo wosatha, mutipatse tonse;
Mutilamulire.

Tsiku ndi Tsiku timalemekeza;
Nanu tikukuzani osaleka;
Mbuye, m’tisunge tingachimwe lero;
M’tichitire nsisi.

Mbuye, chifundo chanu chitigwere;
Monga tikhulupi’ra inu nokha;
Takhulupi’ra zedi mwa’Nu, Mbuye;
Tisagome konse!

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version