Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

  1. Home   »  
  2. Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

 

MBUYE wathu, mutipatsa
Zonse tili nazozo,
Mutikomeratu mtima
Osaleka konseko,
Mutikonda, mutisunga,
Mutisamalira ’fe.

Dzuŵa, madzi, kudya, mpweya,
Moyo, zonse nzanuzi,
Si za ife, nzaulere,
Tingozilandiradi;
Zifumira kwa Aate
Wotikondakondatu.

Monga tilandira, Mbuye,
Mtiphunzitse tonsefe
Tipere chuma chathu
Ndi kusangalalatu;
Zakukhala m’manja mwathu
Tiziyese nzanudi.

Tikhaletu nawo, Mbuye,
Mtima wosauma ’yi
Ndi wofatsa ndi wabwino
Ndi woyerayeradi,
Kuti tiyenere Dzina
La Mbuyathu Yesuyo.

Tisaiwalire ’bale
Athu osadziŵa ’Nu,
Akulira ndi odwala
Tiŵapemphereratu;
Titsanzenso Mbuye Yesu
Ndi k’ŵathangatira ’wo.

Dalitseni, Mbuye, zonse
Zomwe taperekazi,
Mzilandire, nsembe yathu,
Mziyeretse Inudi
Ndi mitima yathu yonse
Tikuyamikirani.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version