Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 390 A! YESU, ndapangana

  1. Home   »  
  2. Hymn 390 A! YESU, ndapangana

Hymn 390 A! YESU, ndapangana

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 390 A! YESU, ndapangana

 

A! YESU, ndapangana
Kutumikira ’Nu
Ndi moyo wanga wonse,
Mbuyanga ndinutu;
Mukhaletu pafupi
Masiku onsewo,
Sindidzaopa konse,
Mutsogolereko.

Ndikufuna kumva Inu,
E, Mawu anuwo,
Ndisamve za satana
Zonyenga zakezo;
Adani anga onse
Andizingiratu;
Mukhaletu pafupi,
Mundithangate ’Nu.

A! Yesu mwapangana
Ndi anthu anuwo
Adzakhala ndinu
Ku Dziko lanulo;
Inenso ndapangana
Ndisabwerere ’yi;
Mndipatse mphamvu yanu
Ambuye ndinudi.

Mundionetse, Yesu,
Mapazi anuwo,
Ndidzapondera awa
Munjira monsemo;
Ndithangateni ine
Ndisalefuke ’yi;
Mundilandire m’Mwamba
Ndikamwaliradi.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version