Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 379 MTSINJE woyerawo

  1. Home   »  
  2. Hymn 379 MTSINJE woyerawo

Hymn 379 MTSINJE woyerawo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 379 MTSINJE woyerawo

 

MTSINJE woyerawo
Wotuluka m’nyumbayo
Ya Mlungu wathuyo
Uyeretse tonsefe.

Ife tifikeko
Tibatizidweko,
Tiyeretsedwedi
Ndi Ambuye leroli.

Mwa anthu onsewo
Umayenda mtsinjewu,
Nuŵachiritsadi
Okhulupirirawo.

Tikondwereratu
Pakumvera Yesuyo,
Abwere onsewo
Ndi kuloŵa m’mtsinjewu.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version