Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 372 DZUŴA la Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 372 DZUŴA la Mulungu

Hymn 372 DZUŴA la Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 372 DZUŴA la Mulungu

 

DZUŴA la Mulungu
Ladzatu labwino;
Ndi chimwemwe ife
Tiliona lero.
Lithaŵitsa nkhaŵa,
Lichotsanso mantha
Ndimo m’mtima mwathu
Likhalitsa bata.

Tikondwera kuti
Tipumula lero;
Tazileka ntchito
Kuti tipemphere.
Koma ntchito zathu
Za palero lino
Nzakumvera Yesu,
Kumlandira bwino.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version