Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

  1. Home   »  
  2. Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

 

KWACHA lero kwati mbee,
Tsiku la Mulunguli;
Dzuŵa liŵaliradi
Thambo ndi zapansipa
Upumira mpweyawu
Wa Mulungu konseku.

M’nyumba yanu, Mlungu, ’yi
Tisonkhana teretu,
Ndi mitundu yonseyi
Tikulambireni ’Nu:
Yesu Mbuye wathuyo
Ndiye Mfumu ponsepo.

Inu Mlungu kalelo
Mutalenga zonsezi
Munapuma tsikulo;
Tipumadi ifenso.
Mommo tilandiratu
Zopumitsa mtimawu.

Yesu munadzukanso
M’manda lero lomwetu;
Ntchito munayambayo
Yakudzutsa anthu ’fe,
Kuti ndi mitimayi
Tigwirebe ntchitozi.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version