Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,

  1. Home   »  
  2. Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,

Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,

 

AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
Lolani kapolo wanu ndikachokere mumtendere;

Chifukwa chipulumutso chanu mwandionetsa zedi,
Chimene munachikonza akachione anthu onse;

Ndi nyali yakuŵalitsa omwe sadziŵa mawu anu;
Ndiwo ulemererowa Israyeli mpingo wanu.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version