Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

 

KODI mwaona chiyani,
Anzeru a kummawa?
Nyenyezi’yo yaoneka,
Isonyeza njirayo.

Mtendere padziko lonse,
Mtendere padziko lonse;
Kwa anthu onse amene,
Alandira Yesuyo.

Nyenyeziyo pooneka,
Isonyeza chikondi;
Kuti Yesu wabadwadi,
Mu kholalo la ng’ombe.

Ndipo iye wolandira,
Ambuye wathu Yesu;
Akhalanso nawo zedi,
Moyowo wochuluka.

Post navigation

Previous: Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
Next: Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 1112 Masiku anga onse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version