Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

  1. Home   »  
  2. Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,

 

PEMPHERO ndiko kufuna,
Kulakalakatu;
Ndi monga moto liyaka
Mumtima wa munthu.

Pemphero ndiko kulira,
Ngakhale misozi,
Kupenyetsetsa Kumwamba,
Mulungu mpafupi.

Pemphero ndiko kufuna
Kwa mwana wamng’ono;
Ndiponso mawu amphamvu
A munthu wamvanu.

Pemphero ndiwo mweyawo
Apuma akristu;
Ndi mapemphero tiloŵa
Dziko la imfalo.

Mutiphunzitse, Mbuyathu,
Kupempha kotero,
Kuyandikira kwa Mlungu
Ndi mtima wabwino.

Post navigation

Previous: Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
Next: Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 630 Ena atsagana nafe
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 130 Tidzakondweradi m’Mwambamo
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version