Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

 

MTIMA wanga ndikonzera,
Mbuye Yesu aitana;
Ati: “Mwana, tapemphera,
Ine sindidzakukana.”

Mbuye ndinu Mfumu yanga
Yolemera ndi yamphamvu;
Ndikapemphatu zambiri,
Simundimanira kanthu.

Ndikabwera nd katundu
Wa zoipa zanga zonse;
Mwazi wake wa Ambuye,
Udzandiyeretsa konse.

Mbuye ndinalema ine,
Mloŵe Inu m’mtima mwanga;
Mkhale m’mwemo mwini wake,
Mantha mwandichotsera ’ne.

Ndine mlendo pansi pano,
Mndilimbitse ndi chikondi;
Bwenzi mundilondolere
Njira pa ulendo wonse.

Mndidziŵitse ntchito yanga,
Mphamvu yake mundipatse;
Mundilimbikitse m’mtima
Ndikhale kwa Atate.

Post navigation

Previous: Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
Next: Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version