Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

 

MTIMA wanga ndikonzera,
Mbuye Yesu aitana;
Ati: “Mwana, tapemphera,
Ine sindidzakukana.”

Mbuye ndinu Mfumu yanga
Yolemera ndi yamphamvu;
Ndikapemphatu zambiri,
Simundimanira kanthu.

Ndikabwera nd katundu
Wa zoipa zanga zonse;
Mwazi wake wa Ambuye,
Udzandiyeretsa konse.

Mbuye ndinalema ine,
Mloŵe Inu m’mtima mwanga;
Mkhale m’mwemo mwini wake,
Mantha mwandichotsera ’ne.

Ndine mlendo pansi pano,
Mndilimbitse ndi chikondi;
Bwenzi mundilondolere
Njira pa ulendo wonse.

Mndidziŵitse ntchito yanga,
Mphamvu yake mundipatse;
Mundilimbikitse m’mtima
Ndikhale kwa Atate.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 1334 Walandira inetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version