Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

 

MTIMA wanga ndikonzera,
Mbuye Yesu aitana;
Ati: “Mwana, tapemphera,
Ine sindidzakukana.”

Mbuye ndinu Mfumu yanga
Yolemera ndi yamphamvu;
Ndikapemphatu zambiri,
Simundimanira kanthu.

Ndikabwera nd katundu
Wa zoipa zanga zonse;
Mwazi wake wa Ambuye,
Udzandiyeretsa konse.

Mbuye ndinalema ine,
Mloŵe Inu m’mtima mwanga;
Mkhale m’mwemo mwini wake,
Mantha mwandichotsera ’ne.

Ndine mlendo pansi pano,
Mndilimbitse ndi chikondi;
Bwenzi mundilondolere
Njira pa ulendo wonse.

Mndidziŵitse ntchito yanga,
Mphamvu yake mundipatse;
Mundilimbikitse m’mtima
Ndikhale kwa Atate.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version