Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

 

KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
Ndadzikundikira chuma Kumwambako;
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye, ndi ‘Nu Bwenzi langa ndithu.
Ndichitenji ngati Kumwamba sikwathu?
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
Mpulumutsi wanga wandikhu’lukira;
Adzandipyoletsa pamene ndafoka,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye watsogola ku Ulemerero,
Ndifuna kugwira dzanja lake konko;
Andidikiranso pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mu Ulemelero tidzakhala m’yaya,
Oyera mtimawo ali kulambira;
Ati: “Aleluya kwa Mlungu wamphamvu,”
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 17 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 772 Muwalimbikitse onse
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version