Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

  1. Home   »  
  2. Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

 

NDAMVATU kuti tifika komweko
Kuli Ambuye, Mtetezi wathuyo.
Ine, pakutha zobvuta zathuzo
Iye tidzamwona maso ndi maso.

Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
Kupenyanso wokondatu;
Tidzakondwera, E, nthaŵi zonsezo
Ndicho chimwemwe ndi ulemutu.

Kaamba chisomo cha Mbuyathu uyu,
Malo okoma tipeza m’Mwambamo;
Kumva mtetezi amene ndi Yesu,
Ndicho chimwemwe ndi chachikulutu.

Onse aliko takonda kalelo,
Kale napita kwa Yesu Mbuyawo;
Koma kumwona Mtetezi wathuyo
Ndicho chimwemwe choposa, nchathucho.

Post navigation

Previous: Hymn 315 YENDANI munjira yake,
Next: Hymn 317 UKATHA moyo wanga

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version