Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

  1. Home   »  
  2. Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

 

NDAMVATU kuti tifika komweko
Kuli Ambuye, Mtetezi wathuyo.
Ine, pakutha zobvuta zathuzo
Iye tidzamwona maso ndi maso.

Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
Kupenyanso wokondatu;
Tidzakondwera, E, nthaŵi zonsezo
Ndicho chimwemwe ndi ulemutu.

Kaamba chisomo cha Mbuyathu uyu,
Malo okoma tipeza m’Mwambamo;
Kumva mtetezi amene ndi Yesu,
Ndicho chimwemwe ndi chachikulutu.

Onse aliko takonda kalelo,
Kale napita kwa Yesu Mbuyawo;
Koma kumwona Mtetezi wathuyo
Ndicho chimwemwe choposa, nchathucho.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 1490 Musachitenso nthantha ‘yi,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version