Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

  1. Home   »  
  2. Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko

 

NDAMVATU kuti tifika komweko
Kuli Ambuye, Mtetezi wathuyo.
Ine, pakutha zobvuta zathuzo
Iye tidzamwona maso ndi maso.

Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
Kupenyanso wokondatu;
Tidzakondwera, E, nthaŵi zonsezo
Ndicho chimwemwe ndi ulemutu.

Kaamba chisomo cha Mbuyathu uyu,
Malo okoma tipeza m’Mwambamo;
Kumva mtetezi amene ndi Yesu,
Ndicho chimwemwe ndi chachikulutu.

Onse aliko takonda kalelo,
Kale napita kwa Yesu Mbuyawo;
Koma kumwona Mtetezi wathuyo
Ndicho chimwemwe choposa, nchathucho.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1164 Tikakhulupira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version