Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

 

NDALIMVA dziko la m’talimo,
Munthu sangathe kulisimba;
Malowo awala koposa,
Ndi Yesu tidzakhala naye.

Komweko, komweko,
Ndi Yesu tidzakhala naye.

Musazengereze anthuni,
Chimwemwe uko chilipodi;
Anthuni, mudzalandiradi,
Ndi Yesu mudzakhala naye.

Mwana’we pereka mtima’ko,
Akuchotsere zoipazo;
Udzakhala wokondweradi,
E! n’kwabwino lola mwana ‘we.

Idzani, mverani, lapani,
Chipulumutso chilipodi;
Kwa Yesu yemwe wofera ‘nu,
Ndi Yesu mudzanka
Kumwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
Next: Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 1362 Mulungu wathu tiyamika,
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version