Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

 

NDALIMVA dziko la m’talimo,
Munthu sangathe kulisimba;
Malowo awala koposa,
Ndi Yesu tidzakhala naye.

Komweko, komweko,
Ndi Yesu tidzakhala naye.

Musazengereze anthuni,
Chimwemwe uko chilipodi;
Anthuni, mudzalandiradi,
Ndi Yesu mudzakhala naye.

Mwana’we pereka mtima’ko,
Akuchotsere zoipazo;
Udzakhala wokondweradi,
E! n’kwabwino lola mwana ‘we.

Idzani, mverani, lapani,
Chipulumutso chilipodi;
Kwa Yesu yemwe wofera ‘nu,
Ndi Yesu mudzanka
Kumwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 1658 Idza wolema,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version