Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

 

NDALIMVA dziko la m’talimo,
Munthu sangathe kulisimba;
Malowo awala koposa,
Ndi Yesu tidzakhala naye.

Komweko, komweko,
Ndi Yesu tidzakhala naye.

Musazengereze anthuni,
Chimwemwe uko chilipodi;
Anthuni, mudzalandiradi,
Ndi Yesu mudzakhala naye.

Mwana’we pereka mtima’ko,
Akuchotsere zoipazo;
Udzakhala wokondweradi,
E! n’kwabwino lola mwana ‘we.

Idzani, mverani, lapani,
Chipulumutso chilipodi;
Kwa Yesu yemwe wofera ‘nu,
Ndi Yesu mudzanka
Kumwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 406 Kwa Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version