Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

  1. Home   »  
  2. Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 302 NDIDZE pafupi pa

 

NDIDZE pafupi pa
Mlungu wanga,
Ngakhale pamtanda
Mundikweza;
Koma ndiimbabe
Mbuye mndikhalitse,
Mbuye mndikhalitse,
M’fupi Ndinu.

Ngakhale kuthengo
Ndasokera,
M’mdima ndigonapa
E, pamwala;
Koma m’kulotako
Ndiyandikizanso,
Ndiyandikizanso
M’fupi Ndinu.

Pajapo ndipenya
Pokwerapo,
Angelo atsika
Kumwambako,
Ndiwo akodola
Kuti ndikabwere,
Kuti ndikabwere
M’fupi Ndinu.

Tsopano poukanso
Wokondwatu,
Ndipeza pomwepo
Pali Mlungu;
Ndipo masautso
Andisendezanso,
Andisendezanso,
M’fupi Ndinu.

Pena pakufadi,
N’kwera m’Mwamba,
Dzuŵa ndi nyenyezi
Zitsalira;
Pomwe ndiimbanso,
Ndidza pafupi pa,
Ndidza pafupi pa
Mlungu wanga.

Post navigation

Previous: Hymn 301 MBUYE, ndapangana
Next: Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version