Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,

 

YEHOVA, Mbusa wangadi,
Ndilibe kusoŵa;
Andigonetsa bwinoli
Mumsipu wokoma.

Ku madzi ake odikha
Anditsogolera;
Ndi moyo wanga wofoka
Aulimbikitsa.

Anditsogolera m’njira
Zakulungamazo;
Chifukwa changa ay’, koma
Cha dzina lakelo.

Ndipyola kodi chikhwaŵa
Cha mthunzi wa imfa?
Ndilibe mantha ngati ’Nu
Mundiperekeza.

Chakudya changa chabwino
Mwandikonzera pha!
Pamaso pa adaniwo
Mudyetsa mtimanga.

Mwadzoza mutu wanga ndi
Mafuta okoma;
Mwadzadza chikho changadi,
Inde, chisefuka.

Zokoma ndi zakuyanja
Zidzanditsatako;
Ndikhala m’nyumba ya Mlungu
Ku nthaŵi zonsezo.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 1195 Wafunafuna ine
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 1194 Padziko lapansi
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version