Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

  1. Home   »  
  2. Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

 

POKONDWA ndi poona vuto
Ndi tsoka pena mwayi,
Ndikumbukira, ndiimbira
Mulungu wangayo.

Kwezani nane Ambuyathu,
Timlemekeze yekha;
Popsinja mtima ndinamtchula,
Nandithangata ’ne

Angelo amazinga nyumba
Za anthu olungama;
Mulungu ateteza omwe
Amkhulupirira.

Laŵani chikondano chake;
Mudzadziŵitsa msanga
Kudala kwawo kwa anake
Omkonda Mbuyeyo.

Opani iye, nimuleke
Kuopa kanthu kena;
Mumtumikire mokondwera,
Akusungani ’nu.

Mulungu wathu Mmodzi yekha
Atate, Mwana, Mzimu,
Akhale ndi ulemerero
Wachikhalirewo!

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version