Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

  1. Home   »  
  2. Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto

 

POKONDWA ndi poona vuto
Ndi tsoka pena mwayi,
Ndikumbukira, ndiimbira
Mulungu wangayo.

Kwezani nane Ambuyathu,
Timlemekeze yekha;
Popsinja mtima ndinamtchula,
Nandithangata ’ne

Angelo amazinga nyumba
Za anthu olungama;
Mulungu ateteza omwe
Amkhulupirira.

Laŵani chikondano chake;
Mudzadziŵitsa msanga
Kudala kwawo kwa anake
Omkonda Mbuyeyo.

Opani iye, nimuleke
Kuopa kanthu kena;
Mumtumikire mokondwera,
Akusungani ’nu.

Mulungu wathu Mmodzi yekha
Atate, Mwana, Mzimu,
Akhale ndi ulemerero
Wachikhalirewo!

Post navigation

Previous: Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
Next: Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version