Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

 

AMBUYE m’chipululu,
Analefuka ndi njala;
Polowa m’mayesero,
Anagonjetsatu Satana.
M’dziko lapansi lero lino,
Alipo omutsata,
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Nyamulani maso anu,
Muyang’ane m’kati mwanu;
Alipo anthu ena,
Oyitanidwa, nasankhidwa.
Mutawayang’ana iwo,
Akunga a umphawi;
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Kuwachotsa kwa Mbuye,
Satanayo walephera;
Powazunza iwotu,
Achiyesa chimwemwe ndithu.
Ambuye nawalimbikitsa,
Napukuta misozi;
Nawalonjeza koronayo,
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Akhrisitu tilimbike,
Kugwira ntchito ya Mbuye;
Timvere mawu ake,
Tidzagonjetsatu Satana.
Pomalizatu moyo uno,
Tidzapita Kumwamba;
Tidzayimbira Mulunguyo,
Ndife mbewu zosawonongeka.

Post navigation

Previous: Hymn 282 INU muli mehere,
Next: Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 351 Titi bwanji?
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 307 Atate Wamkulu ndi wamphamvu zonse,
  • Hymn 1513 M’Bukuli ine ndi
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version