Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

 

AMBUYE m’chipululu,
Analefuka ndi njala;
Polowa m’mayesero,
Anagonjetsatu Satana.
M’dziko lapansi lero lino,
Alipo omutsata,
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Nyamulani maso anu,
Muyang’ane m’kati mwanu;
Alipo anthu ena,
Oyitanidwa, nasankhidwa.
Mutawayang’ana iwo,
Akunga a umphawi;
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Kuwachotsa kwa Mbuye,
Satanayo walephera;
Powazunza iwotu,
Achiyesa chimwemwe ndithu.
Ambuye nawalimbikitsa,
Napukuta misozi;
Nawalonjeza koronayo,
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Akhrisitu tilimbike,
Kugwira ntchito ya Mbuye;
Timvere mawu ake,
Tidzagonjetsatu Satana.
Pomalizatu moyo uno,
Tidzapita Kumwamba;
Tidzayimbira Mulunguyo,
Ndife mbewu zosawonongeka.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version