Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

  1. Home   »  
  2. Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

 

AMBUYE ngwodalitsika,
Mulungu wa Israyeli ndiye,
Poti anayang’ana naŵawombola anthu ake,

Napulumutsa tonse mwapfuko la Davide mwana wake;
Monga analankhula mwa aneneri ake,

Adzatipulumutsa kudzanja la onse akutida,
Ndipo adzachitira akulu chifundo ndi chisoni.

Ndiye akumbukira pangani loyera lake lija,
Ndi chilumbiro chake cha kwa atate Abrahamu,

Choti timtumikire osaŵaopa ’dani athu,
Ndi kuyeranso mtima mwa chilungamo nsiku zonse.

Mwana, adzakuyesa mneneritu wa Wamkulukulu,
Ndiwe udzakonzera njira ya Mbuye Wakumwamba.

Udzadziŵitsa anthu za Mpulumutsi wawo yemwe
Aŵakhululukira
Nafafaniza tchimo lawo,

Poti Mulungu wathu ali ndi mtima wachifundo.
Ndiye kumwamba komwe
Ationetsa mbanda kucha,

Poŵalitsira omwe ali mumdima ndi muimfa,
Ndi potilunjikitsa tonse munjira yamtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version