Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

  1. Home   »  
  2. Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,

 

AMBUYE ngwodalitsika,
Mulungu wa Israyeli ndiye,
Poti anayang’ana naŵawombola anthu ake,

Napulumutsa tonse mwapfuko la Davide mwana wake;
Monga analankhula mwa aneneri ake,

Adzatipulumutsa kudzanja la onse akutida,
Ndipo adzachitira akulu chifundo ndi chisoni.

Ndiye akumbukira pangani loyera lake lija,
Ndi chilumbiro chake cha kwa atate Abrahamu,

Choti timtumikire osaŵaopa ’dani athu,
Ndi kuyeranso mtima mwa chilungamo nsiku zonse.

Mwana, adzakuyesa mneneritu wa Wamkulukulu,
Ndiwe udzakonzera njira ya Mbuye Wakumwamba.

Udzadziŵitsa anthu za Mpulumutsi wawo yemwe
Aŵakhululukira
Nafafaniza tchimo lawo,

Poti Mulungu wathu ali ndi mtima wachifundo.
Ndiye kumwamba komwe
Ationetsa mbanda kucha,

Poŵalitsira omwe ali mumdima ndi muimfa,
Ndi potilunjikitsa tonse munjira yamtendere.

Post navigation

Previous: Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
Next: Hymn 29 CHIKONDI cha

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1392 Mlungu kuona athiratu
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version