Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

  1. Home   »  
  2. Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

 

MKRISTU, ulimbike
M’ntchito yakeyo;
Yesu anafera
Anthu akewo.

Mphamvu zathu zonse
Tionetsenso,
Kuti kudziŵike
Tili akewo.

Mtima wakufatsa
Amakondako;
Ndipo anthu onse
Angatengero.

Mapemphero athu
Tikakwezebe,
Dzina lake lomwe
Tiyamike ’fe.

Limbikani nonse
Mpaka imfayo.
Ndipo Mfumu yathu
Idzakondwatu.

Post navigation

Previous: Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
Next: Hymn 277 GWIRA zintchito zako,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version