Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

  1. Home   »  
  2. Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 276 MKRISTU, ulimbike

 

MKRISTU, ulimbike
M’ntchito yakeyo;
Yesu anafera
Anthu akewo.

Mphamvu zathu zonse
Tionetsenso,
Kuti kudziŵike
Tili akewo.

Mtima wakufatsa
Amakondako;
Ndipo anthu onse
Angatengero.

Mapemphero athu
Tikakwezebe,
Dzina lake lomwe
Tiyamike ’fe.

Limbikani nonse
Mpaka imfayo.
Ndipo Mfumu yathu
Idzakondwatu.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 1779 M’dzikomo Ambuye
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version