Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

  1. Home   »  
  2. Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

 

KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
Werengani Mawu masiku onsewo.
Uthenga omwe ali akufoka,
Madalitso ake ufunefunebe.

Khalani woyera, dziko laipadi;
Pemphera kolimba kwa Yesu
Mbuyathu.
Yang’anitsa Yesu ndi kumutsatira,
Kuti anthu ena aonenso Iye.

Khalatu woyera, akutsogozetu;
Usamtsogolere munjira zakozo.
Pokondwa ndi m’nsoni tsata Ambuyako
Khulupira Yesu ndi Mawu akewo.

Khalatu woyera, khalatu wofatsa;
Alilamulire ganizo lakolo.
Utatsogozedwa ndi Mzimu wakeyo,
Msanga udzagwira m’Mwamba ntchito yake.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version