Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

  1. Home   »  
  2. Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;

 

KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
Werengani Mawu masiku onsewo.
Uthenga omwe ali akufoka,
Madalitso ake ufunefunebe.

Khalani woyera, dziko laipadi;
Pemphera kolimba kwa Yesu
Mbuyathu.
Yang’anitsa Yesu ndi kumutsatira,
Kuti anthu ena aonenso Iye.

Khalatu woyera, akutsogozetu;
Usamtsogolere munjira zakozo.
Pokondwa ndi m’nsoni tsata Ambuyako
Khulupira Yesu ndi Mawu akewo.

Khalatu woyera, khalatu wofatsa;
Alilamulire ganizo lakolo.
Utatsogozedwa ndi Mzimu wakeyo,
Msanga udzagwira m’Mwamba ntchito yake.

Post navigation

Previous: Hymn 263 AMBUYE mundisunge
Next: Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hello world!
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version