Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

 

M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
Ndiyenderane nanu;
E, nditsamire pa ‘nu Yesu,
Panjira yonseyi.

Ndiwonetsere kuunika,
Kokoma kwanu Yesu!
Yabwino mbiri ndibukitse,
Yokondweretsayo.

Chitsime chakuyera ine,
Ndifananetu nacho;
Mundigwiritse ntchito zanu,
E, zanu zokhazo.

Mulamulire mtima, Yesu,
Ndi chifuniro changa;
Mulowe mwanga ngati Mfumu;
Kuti ndimvere ‘Nu.

Ndimamva njala kuno, Yesu,
Yakufunitsa Inu;
Kumwamba kwanu ndikukhumba.
Kukondwa nanuko.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 1505 Ndikampeza, ndikamtsata
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version