Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

  1. Home   »  
  2. Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

 

MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
(Yesu) Yemwe anafera ine,
Ndiye anandiwombola;
Yesu, Yesu.

Mwazi wake ndi chitsime changa,
(Yesu) Pamene ndikasambamo
Zochimwa zanga zidzatha;
Yesu, Yesu.

Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
(Yesu) ngati mundisiya ndekha,
Kukhala ndekha sinditha;
Yesu, Yesu.

Yesu Mfumu, ine ndisekere
(Yesu) Inu Mpulumutsi wanga
Pamene mukhala nane;
Yesu, Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 1511 Mndidalitsere ‘ne
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version