Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

  1. Home   »  
  2. Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

 

MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
(Yesu) Yemwe anafera ine,
Ndiye anandiwombola;
Yesu, Yesu.

Mwazi wake ndi chitsime changa,
(Yesu) Pamene ndikasambamo
Zochimwa zanga zidzatha;
Yesu, Yesu.

Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
(Yesu) ngati mundisiya ndekha,
Kukhala ndekha sinditha;
Yesu, Yesu.

Yesu Mfumu, ine ndisekere
(Yesu) Inu Mpulumutsi wanga
Pamene mukhala nane;
Yesu, Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
Next: Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hello world!
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 1502 Kodi ulikulemedwa
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version