Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

  1. Home   »  
  2. Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI

 

MWAKHULUPIRIRADI
Yesu Ambuyathu;
Muli nazo zakezo,
Zidzatu zinanso.
Mlungu wachisomocho
Mbuye wathu ndiye,
Ati zinthu zonsezo
Nzathu mwa Iyeyo.

(Zina ndi zinanzo
Zidza kwa ifedi,
Inde mtima wakewo
Uli wokomadi.)

Mwamva Yesu m’mtimamo,
Adzanso kaŵiri,
M’mene ali nanutu
Muli ndi Chimwemwe.
Ntchito zachifundozi
Iye watha izi,
Kuti mwawo m’Mwambamo
Naye tikhalebe.

Mwamva Mzimu wakewo,
Zake zimvekanso
Kugwa ngati mvulayo
Yachisomo chake.
Mzimu ndiye mphamvudi
M’moyo mwathu muno,
Mpaka tidzafikako
Komwe kuli Yesu

Post navigation

Previous: Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
Next: Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 1781 Timwimbire nyimbo,
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1263 Mbuye, ndingogonj tere, Ndibvomerapo;
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version