Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

  1. Home   »  
  2. Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

 

INE ndili ndi manyazi
Kuti kale lomwelo
Ndinanyoza kudza komwe
Kwa Mtetezi wanga Yesu,
Ndati, Sindimfuna `yi.

Koma Iye wandipeza;
Ndamuona m`mtandamo,
Mwa kufera ine momwe;
Ndipo ndati m`mtima mwanga:
Mbuye, ndikufunani.

Nsiku zonse kwanja kwake
Kunandithandizatu,
Kunandichiritsa mtima;
Ndipo ndati: Mpulumutsi,
Ndinu Mbuye wangatu.

Sindifuna Mbuye wina,
Koma Yesu yekhayo;
Ine ndili munthu wake,
Iye anandigonjetsa
Ndi kukonda kwakeko.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version