Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

  1. Home   »  
  2. Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 213 INE ndili ndi manyazi

 

INE ndili ndi manyazi
Kuti kale lomwelo
Ndinanyoza kudza komwe
Kwa Mtetezi wanga Yesu,
Ndati, Sindimfuna `yi.

Koma Iye wandipeza;
Ndamuona m`mtandamo,
Mwa kufera ine momwe;
Ndipo ndati m`mtima mwanga:
Mbuye, ndikufunani.

Nsiku zonse kwanja kwake
Kunandithandizatu,
Kunandichiritsa mtima;
Ndipo ndati: Mpulumutsi,
Ndinu Mbuye wangatu.

Sindifuna Mbuye wina,
Koma Yesu yekhayo;
Ine ndili munthu wake,
Iye anandigonjetsa
Ndi kukonda kwakeko.

Post navigation

Previous: Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
Next: Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version