Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

  1. Home   »  
  2. Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

 

AMBUYE’naitan’ne;
“Dzapumulire kuno,
Tsamira mutu, mwana’we
M’chifuwa mwanga muno.”

Ndabwera kwa Ambuyeyo;
Wolema, wachisoni;
Anandipulumutsako,
Nakondweretsa ine.

Ambuye naitana’ne;
“Ndipatsa anthu madzi,
Wotopa ndi waludzu’we
Dzamwere moyo kuno.”

Ndabwera kwa Ambuyeyo.
Ndamwera madzi awa;
Laleka ndithu ludzulo,
Tsopano moyo wadza

Ambuye naitana’ne;
“La dziko ndine Dzuŵa,
Yang’ana Ine, kwacha’we,
Wachoka mdima uja.”

Ndayang’anira Mbuyeyo
Ndzapeza Dzuŵa langa
Londiyendetsa bwinoli
Pa njira yanga yonse.

Post navigation

Previous: Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Next: Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 563 Ndipo Mwana uyu Yesu
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version