Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

 

LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
Musekerere kuti tidzaimbira Yesu.
Imbira!
Timwimbire Yesu,
Mpulumutsi wathu!

Imbira!
Timwimbire Yesu,
Tonse tidzakondwera.

Musadziunjikire chuma cha padziko
Dzimbiri ndi njenjete
zimachiononga.

Koma mudziunjikire chuma cha Kumwamba
Kumene anapita Mtsogoleri wanu.

Aliponso adani am’kati ndi akunja;
Yesu watisekera, tidzakuimbirani.

Aliponse mabvuto, ena ndi oipa;
Yesu mutimasule kwa adani athu.

Post navigation

Previous: Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Next: Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 1031 Gwira zintchito zako,
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version