Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,

 

LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
Musekerere kuti tidzaimbira Yesu.
Imbira!
Timwimbire Yesu,
Mpulumutsi wathu!

Imbira!
Timwimbire Yesu,
Tonse tidzakondwera.

Musadziunjikire chuma cha padziko
Dzimbiri ndi njenjete
zimachiononga.

Koma mudziunjikire chuma cha Kumwamba
Kumene anapita Mtsogoleri wanu.

Aliponso adani am’kati ndi akunja;
Yesu watisekera, tidzakuimbirani.

Aliponse mabvuto, ena ndi oipa;
Yesu mutimasule kwa adani athu.

Post navigation

Previous: Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
Next: Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1830 Ndiye M’busa wanga
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 1824 Mulungu wathu Mmodzi yekha
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version