Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

 

AITANA, aitana dziko lonse,
Imvani mukhaliranji chete?
Aitana,
Aitana aitana dziko lonse.

Mfumu iyi, Mfumu iyi ya Kumwamba
Ndi Yesu, ndi Mpulumutsiyo wa anthu onse.
Anthu onse, anthu onse, tinke kwawo.

Aitana,aitana inu mayi,
Ndi Yesu, amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu mayi.

Aitana, aitana inu ’tate,
Ndi Yesu amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu ’tate.

Yesu ati, Yesu ati; “Muzisiye
Zoipa zimene muzichita, muzisiye,
Muzisiye, muzisiye inu nonse.”

Titi bwanji? Titi bwanji ife anthu?
Ndi Yesu anatifera ife akuchimwa;
Akuchimwa, akuchimwa tinke kwawo.

Post navigation

Previous: Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
Next: Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version