Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,

 

AITANA, aitana dziko lonse,
Imvani mukhaliranji chete?
Aitana,
Aitana aitana dziko lonse.

Mfumu iyi, Mfumu iyi ya Kumwamba
Ndi Yesu, ndi Mpulumutsiyo wa anthu onse.
Anthu onse, anthu onse, tinke kwawo.

Aitana,aitana inu mayi,
Ndi Yesu, amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu mayi.

Aitana, aitana inu ’tate,
Ndi Yesu amene anakhetsa mwazi wake;
Mwazi wake unagwera inu ’tate.

Yesu ati, Yesu ati; “Muzisiye
Zoipa zimene muzichita, muzisiye,
Muzisiye, muzisiye inu nonse.”

Titi bwanji? Titi bwanji ife anthu?
Ndi Yesu anatifera ife akuchimwa;
Akuchimwa, akuchimwa tinke kwawo.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version