Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

 

SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
Pali anthu otayika, masiku alikutha;
Ngati tikondwerera,
Pakuyenda ulendowu,
Tonse tidzachita bwino, masiku alikutha.

Akutha, akutha, masiku akutha,
Tonse tichitetu bwino, masiku ali kutha.

Tisakhale awulesi, masiku alikutha,
Nkhope zathu zikondwere, masiku alikutha;
Dziko ili ndi lochimwa, lodzaza ndi chisoni,
Thangatani akugwawo, masiku alikutha.

Tamangidwa ndi unyolo, masiku alikutha,
Tisiyetu zoipazi, masiku alikutha;
Tonsefe muzabwinotu
Tidzakhala ndi Mlungu;
Ndipo tidzakondweradi mu nthawi zamuyaya,

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 412 MOYO uli pafupi,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 225 NDIDZAIMBA za Mulungu,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 425 AKRISTU ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version