Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

  1. Home   »  
  2. Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,

 

SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
Pali anthu otayika, masiku alikutha;
Ngati tikondwerera,
Pakuyenda ulendowu,
Tonse tidzachita bwino, masiku alikutha.

Akutha, akutha, masiku akutha,
Tonse tichitetu bwino, masiku ali kutha.

Tisakhale awulesi, masiku alikutha,
Nkhope zathu zikondwere, masiku alikutha;
Dziko ili ndi lochimwa, lodzaza ndi chisoni,
Thangatani akugwawo, masiku alikutha.

Tamangidwa ndi unyolo, masiku alikutha,
Tisiyetu zoipazi, masiku alikutha;
Tonsefe muzabwinotu
Tidzakhala ndi Mlungu;
Ndipo tidzakondweradi mu nthawi zamuyaya,

Post navigation

Previous: Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
Next: Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version