Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 118 PANALI munthu amene,

  1. Home   »  
  2. Hymn 118 PANALI munthu amene,

Hymn 118 PANALI munthu amene,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 118 PANALI munthu amene,

 

PANALI munthu amene,
Analimbana ndi mngelo;
Kufikira mbandakucha:
“Sindidzakusiya.”

(M) Ndipo mngelo anati:
(O) “Yakobo iwe, ndisiye;
Kunja kuli kucha, ndisiye,
“Sindidzakusiya!”

Pomwepo mngelo ‘nafunsa:
“Dzina ndi yani?”
“Yakobo,’
“Dzina ndi yani?”
“Yakobo,
Sindidzakusiya.”

Ndipo Mulungu afuna,
Tigwire ntchito yakeyo;
Yolimbana ndi zoipa,
Zodetsa m’mtimamo.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version