Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 118 PANALI munthu amene,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 118 PANALI munthu amene,

 

PANALI munthu amene,
Analimbana ndi mngelo;
Kufikira mbandakucha:
“Sindidzakusiya.”

(M) Ndipo mngelo anati:
(O) “Yakobo iwe, ndisiye;
Kunja kuli kucha, ndisiye,
“Sindidzakusiya!”

Pomwepo mngelo ‘nafunsa:
“Dzina ndi yani?”
“Yakobo,’
“Dzina ndi yani?”
“Yakobo,
Sindidzakusiya.”

Ndipo Mulungu afuna,
Tigwire ntchito yakeyo;
Yolimbana ndi zoipa,
Zodetsa m’mtimamo.

Exit mobile version