Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 113 KALERO anthu onse

  1. Home   »  
  2. Hymn 113 KALERO anthu onse

Hymn 113 KALERO anthu onse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 113 KALERO anthu onse

 

KALERO anthu onse
Nachimwa kwa Mulungu
Mulungu anawona
Nawona tchimo lawo,
Nafuna kwawononga,
Nafuna kwawononga.

Mulungu anatuma,
Natuma mvula ija,
Nadzaza dziko lonse
Anafa anthu onse,
Anafa m’mvula muja,
Anafa m’mvula muja.

Mulungu anatuma,
Natuma Nowa uja,
Wamanga chombo chake,
Ndi chachitalitali,
Nowayo nayendamo,
Nowayo nayendamo.

Nowayo anatuma,
Natuma chikwangwala,
Chatsika pansi pansi,
Chosabwerera konse,
Chithaŵa m’talitali,
Chithaŵa m’talitali.

Kutuma wabwereza,
Natuma nkhunda ija,
Yatsika pamadzipo,
Yathyolatu mayani,
Yampatsa Nowa yemwe,
Yampatsa Nowa yemwe.

Kalelo Mbuye Yesu
’Nafera anthu onse,
Ndiyeyo chombo chathu,
Tikabisala mommo
Tipulumuka mommo,
Tipulumuka mommo.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 855 Aulendo amayenda

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version