Hymn 688 Anthu akum’mawa December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Believers Christian Hymns Chichewa Believers Christian Hymns Hymn 688 Anthu akum’mawa Anthu akum’mawa Nanka msangako, Nzure ‘nali nazo, Nafatsansowo; Nanka kuli Mwana Anabadwayo; Anatsogozedwa Ndi nyenyeziyo.