Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

  1. Home   »  
  2. Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

 

NDIKONDA mbiri yomwe
Ya amithengawo
Ya Mbuye, Mfumu yathu
Pofika pansipa;
Zochimwa zindizinga,
Koma ndidziŵatu
Anawombola ine
Pakundikondadi.

Ndikondwa kuti Yesu ’Nakhala mwanatu,
Chitsanzo atipatsa
Cha moyo wakewo;
Ndikati ndimtsatire
Zochita zakezo,
Sadzandinyoza konse
Pakundikondadi.

Pakumyamika Iye
Ndidzamwimbiratu;
Ngakhale sindimwona
Amandimveradi;
Pakuti walonjeza
Adzalandira ’ne
Ndiimbe ndi angelo,
Pakundikondadi.

Post navigation

Previous: Hymn 468 NDIKONDWA kuti
Next: Hymn 470 YESU andikonda ine,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 239 Akumwambawo
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 158 WOCHIMWA iwe, bweratu,
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 1772 Iye amakhutitsa
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version