Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

  1. Home   »  
  2. Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

 

NDIKONDA mbiri yomwe
Ya amithengawo
Ya Mbuye, Mfumu yathu
Pofika pansipa;
Zochimwa zindizinga,
Koma ndidziŵatu
Anawombola ine
Pakundikondadi.

Ndikondwa kuti Yesu ’Nakhala mwanatu,
Chitsanzo atipatsa
Cha moyo wakewo;
Ndikati ndimtsatire
Zochita zakezo,
Sadzandinyoza konse
Pakundikondadi.

Pakumyamika Iye
Ndidzamwimbiratu;
Ngakhale sindimwona
Amandimveradi;
Pakuti walonjeza
Adzalandira ’ne
Ndiimbe ndi angelo,
Pakundikondadi.

Post navigation

Previous: Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 94 KHAMULO liliko
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version