Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!

  1. Home   »  
  2. Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!

Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!

 

USIKUWO, woyerawo!
Mwana adam’lerayo;
Akakhale Mfumuyo,
Anabadwa m’kholamo,
Mfumu ya mafumu,
Ndi ya anthuwo.

Mwanayo wa Mlunguyo,
Andikonda inetu;
Nan’tayira chumacho,
Nadzagona mu’dzumo,
Ndiyamika Mbuye,
Wanga Yesuyo.

Usikuwo, woyerawo!
Wadzatu mtenderewo;
Ife tonse anthuwo,
Atitenga Mlunguyo,
M’lemekeze “Tate,
Mwana, Mzimunso.

Post navigation

Previous: Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
Next: Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 170 YESU ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 419 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 824 Yesu mutipatse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version