Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

  1. Home   »  
  2. Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira

 

TIIMBE ndi kulalikira
Mthenga wa chikondicho
Anamva Mlungu m’Mwambamo
Kulira kwathu pansipa.

(Ndikhulupirira Yesu
Wobadwira m’kholamo;
Iye ndiye Mfumu yathu,
Timtame nthaŵi zonse.)

Kwa ife lero anabadwa
Mwana wa Mariyayo,
Pamsinkhu, ine mng’ono koma
Mwini dziko lonseli.

Anadza nazo mphatso zake
Anatikonzeratu; Anatitseguliradi
Pakhome pa Ufumuwo.

Ambuye takutamandani
Tsiku lakubadwali,
Mwa Inu tonse tikondwera,
Tiseke tonsefe.

A! Yesu Mbuye wakuyera,
Munagona m’kholamo;
Mudzikonzere leronso
Mogona m’mtima mwangamu.

Ulemerero m’Mwambamwamba
Ndi mtendere pansipa;
Tiimbe nafe nyimboyi,
Timyamikire Mbuyathu

(Yesu ndiye Mfumu,
Yesu ndiye Mfumu!
Ndikhulupirira Yesu wobadwira m’kholamo.)

Post navigation

Previous: Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
Next: Hymn 461 ANA inu, myamikeni

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 716 Tibwezeretu bwanjiko?
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version