Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

 

YEHOVA Mlungu wathu,
Amene mumapatsa
Zipatso za chikondi
Polenga anthu anu,
Mupatse awa ‘ŵiri
Mitima yokondwetsa,
Yofana m’munda muja
Munayendamo kale.

Mbuyathu wokondedwa,
Pokhala m’dziko muno
Munadza ku ukwati,
Naŵadalitsa onse;
Ukwatiwu mukonze,
Mukhale nafe pano;
Iwowa m’ŵadalitse
M’chifundo chanu chonse.

Ndi Mzimutu Woyera
Mufike nayo mphamvu,
Mukatsangane nawo
Akupangana omwe;
Mupatse ’wo chisomo
Chokometsetsa mtima;
Chikuletu chikondi
Chitsazo nchanu chomwe.

Mulungu mwa Atatu,
Atate, Mwana, Mzimu,
Tikhaletu wokondwa
Ndi Inu m’chiyanjano;
Titama Inu Mlungu,
Wokonda ife ndinu;
M’ulendo wathu wonse
Tiyende m’chikondano.

Post navigation

Previous: Hymn 435 ANAKWATIRA kale
Next: Hymn 437 MULUNGU wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version