Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,

 

YEHOVA Mlungu wathu,
Amene mumapatsa
Zipatso za chikondi
Polenga anthu anu,
Mupatse awa ‘ŵiri
Mitima yokondwetsa,
Yofana m’munda muja
Munayendamo kale.

Mbuyathu wokondedwa,
Pokhala m’dziko muno
Munadza ku ukwati,
Naŵadalitsa onse;
Ukwatiwu mukonze,
Mukhale nafe pano;
Iwowa m’ŵadalitse
M’chifundo chanu chonse.

Ndi Mzimutu Woyera
Mufike nayo mphamvu,
Mukatsangane nawo
Akupangana omwe;
Mupatse ’wo chisomo
Chokometsetsa mtima;
Chikuletu chikondi
Chitsazo nchanu chomwe.

Mulungu mwa Atatu,
Atate, Mwana, Mzimu,
Tikhaletu wokondwa
Ndi Inu m’chiyanjano;
Titama Inu Mlungu,
Wokonda ife ndinu;
M’ulendo wathu wonse
Tiyende m’chikondano.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 1321 Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version