Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

 

MUNDIMVERE, Mbuye wanga
Nkana ine ndimalakwa,
Koma ndinu moyo wanga;
Mbuye, mkhale ndine.

Ndine mlendo pansi pano,
Msanditaye m’dzanja lanu,
Mundisunge mwana wanu;
Mbuye, mkhale ndine.

Munafera ine kale
Kuti mukandimasule,
Lero lino mndinyamule;
Mbuye, mkhale ndine.

Mundidzaze ndi chikondi,
Mndiyeretse m’mtima monse,
Chifuniro changa mthyole;
Mbuye, mkhale ndine.

Imfa ikandifikira,
Inu ndidzakangamira
Ndikaloŵa ine m’mdima,
Mbuye, mkhale ndine.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version