Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga

 

MUNDIMVERE, Mbuye wanga
Nkana ine ndimalakwa,
Koma ndinu moyo wanga;
Mbuye, mkhale ndine.

Ndine mlendo pansi pano,
Msanditaye m’dzanja lanu,
Mundisunge mwana wanu;
Mbuye, mkhale ndine.

Munafera ine kale
Kuti mukandimasule,
Lero lino mndinyamule;
Mbuye, mkhale ndine.

Mundidzaze ndi chikondi,
Mndiyeretse m’mtima monse,
Chifuniro changa mthyole;
Mbuye, mkhale ndine.

Imfa ikandifikira,
Inu ndidzakangamira
Ndikaloŵa ine m’mdima,
Mbuye, mkhale ndine.

Post navigation

Previous: Hymn 390 A! YESU, ndapangana
Next: Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version