Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 390 A! YESU, ndapangana

  1. Home   »  
  2. Hymn 390 A! YESU, ndapangana

Hymn 390 A! YESU, ndapangana

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 390 A! YESU, ndapangana

 

A! YESU, ndapangana
Kutumikira ’Nu
Ndi moyo wanga wonse,
Mbuyanga ndinutu;
Mukhaletu pafupi
Masiku onsewo,
Sindidzaopa konse,
Mutsogolereko.

Ndikufuna kumva Inu,
E, Mawu anuwo,
Ndisamve za satana
Zonyenga zakezo;
Adani anga onse
Andizingiratu;
Mukhaletu pafupi,
Mundithangate ’Nu.

A! Yesu mwapangana
Ndi anthu anuwo
Adzakhala ndinu
Ku Dziko lanulo;
Inenso ndapangana
Ndisabwerere ’yi;
Mndipatse mphamvu yanu
Ambuye ndinudi.

Mundionetse, Yesu,
Mapazi anuwo,
Ndidzapondera awa
Munjira monsemo;
Ndithangateni ine
Ndisalefuke ’yi;
Mundilandire m’Mwamba
Ndikamwaliradi.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version