Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 379 MTSINJE woyerawo

  1. Home   »  
  2. Hymn 379 MTSINJE woyerawo

Hymn 379 MTSINJE woyerawo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 379 MTSINJE woyerawo

 

MTSINJE woyerawo
Wotuluka m’nyumbayo
Ya Mlungu wathuyo
Uyeretse tonsefe.

Ife tifikeko
Tibatizidweko,
Tiyeretsedwedi
Ndi Ambuye leroli.

Mwa anthu onsewo
Umayenda mtsinjewu,
Nuŵachiritsadi
Okhulupirirawo.

Tikondwereratu
Pakumvera Yesuyo,
Abwere onsewo
Ndi kuloŵa m’mtsinjewu.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 1456 Pakuti anthu akumvera
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version