Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 379 MTSINJE woyerawo

  1. Home   »  
  2. Hymn 379 MTSINJE woyerawo

Hymn 379 MTSINJE woyerawo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 379 MTSINJE woyerawo

 

MTSINJE woyerawo
Wotuluka m’nyumbayo
Ya Mlungu wathuyo
Uyeretse tonsefe.

Ife tifikeko
Tibatizidweko,
Tiyeretsedwedi
Ndi Ambuye leroli.

Mwa anthu onsewo
Umayenda mtsinjewu,
Nuŵachiritsadi
Okhulupirirawo.

Tikondwereratu
Pakumvera Yesuyo,
Abwere onsewo
Ndi kuloŵa m’mtsinjewu.

Post navigation

Previous: Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
Next: Hymn 380 ATATE, muwapenya

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 38 ANGELO ayimba,
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version