Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 372 DZUŴA la Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 372 DZUŴA la Mulungu

Hymn 372 DZUŴA la Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 372 DZUŴA la Mulungu

 

DZUŴA la Mulungu
Ladzatu labwino;
Ndi chimwemwe ife
Tiliona lero.
Lithaŵitsa nkhaŵa,
Lichotsanso mantha
Ndimo m’mtima mwathu
Likhalitsa bata.

Tikondwera kuti
Tipumula lero;
Tazileka ntchito
Kuti tipemphere.
Koma ntchito zathu
Za palero lino
Nzakumvera Yesu,
Kumlandira bwino.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 1706 Pamutu minga kwe!
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 1207 Poyambapo ndakondwadi,
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version