Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

 

NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Amva pemphero ndi kulira kwanga,
Namachereza khutu nditapfuula,
Andithandiza, nandipulumutsa.

Mulungu wanga ndiye wachifundo
Ndi wolungama mtima ndi wabwino;
Apulumutsa anthu akufoka,
Akathandiza nkhaŵa imachoka.

Mtimanga, bwera kuti upumule,
Wakuchitiranso zokoma Mbuye,
Wakuchotsera imfa ndi misozi,
Ndingakhumudwe asungira phazi.

Nditani ine kubwezera Mbuye
Zokoma zonse anandichitira?
Chipulumutso chake ndidzatama,
Ndinalumbira zija ndidzapatsa.

Imfa ya anthu ake imkomera,
Aŵalandira m’nyumba zokonzeka.
Mbuye, kapolo wanu ndipereka
Nsembeyi yonga yanu, ndine ndekha.

Post navigation

Previous: Hymn 319 NDIDZATANI ine,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version