Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

  1. Home   »  
  2. Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga

 

NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Amva pemphero ndi kulira kwanga,
Namachereza khutu nditapfuula,
Andithandiza, nandipulumutsa.

Mulungu wanga ndiye wachifundo
Ndi wolungama mtima ndi wabwino;
Apulumutsa anthu akufoka,
Akathandiza nkhaŵa imachoka.

Mtimanga, bwera kuti upumule,
Wakuchitiranso zokoma Mbuye,
Wakuchotsera imfa ndi misozi,
Ndingakhumudwe asungira phazi.

Nditani ine kubwezera Mbuye
Zokoma zonse anandichitira?
Chipulumutso chake ndidzatama,
Ndinalumbira zija ndidzapatsa.

Imfa ya anthu ake imkomera,
Aŵalandira m’nyumba zokonzeka.
Mbuye, kapolo wanu ndipereka
Nsembeyi yonga yanu, ndine ndekha.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 563 Ndipo Mwana uyu Yesu
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version