Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,

 

NDALIMVA dziko la m’talimo,
Munthu sangathe kulisimba;
Malowo awala koposa,
Ndi Yesu tidzakhala naye.

Komweko, komweko,
Ndi Yesu tidzakhala naye.

Musazengereze anthuni,
Chimwemwe uko chilipodi;
Anthuni, mudzalandiradi,
Ndi Yesu mudzakhala naye.

Mwana’we pereka mtima’ko,
Akuchotsere zoipazo;
Udzakhala wokondweradi,
E! n’kwabwino lola mwana ‘we.

Idzani, mverani, lapani,
Chipulumutso chilipodi;
Kwa Yesu yemwe wofera ‘nu,
Ndi Yesu mudzanka
Kumwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
Next: Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 1170 Pamtanda wake
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version